Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 42:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Taonani, zinthu zimene ndinaneneratu kalekale zachitika,

      Tsopano ndikulengeza zinthu zatsopano.

      Zisanayambe kuonekera, ndimakuuzani.”+

  • Yesaya 45:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Lankhulani ndipo mufotokoze mlandu wanu.

      Mukambirane mogwirizana.

      Kodi ndi ndani ananeneratu zimenezi kalekale

      Nʼkuzilengeza kuyambira kalekale?

      Kodi si ine, Yehova?

      Palibenso Mulungu wina koma ine ndekha.

      Ine ndi Mulungu wolungama komanso Mpulumutsi+ ndipo palibenso wina kupatulapo ine.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena