-
Yeremiya 33:25, 26Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
25 Yehova wanena kuti, ‘Mofanana ndi mmene ndinakhazikitsira pangano langa loti kukhale masana ndi usiku,+ malamulo akumwamba ndi dziko lapansi,+ 26 sindidzakananso mbadwa* za Yakobo ndi za Davide mtumiki wanga, kuti pakati pa mbadwa* zake ndisatengepo olamulira ana a Abulahamu,* Isaki ndi Yakobo. Chifukwa ndidzasonkhanitsa anthu onse amene anatengedwa kupita kudziko lina+ ndipo ndidzawamvera chisoni.’”+
-