Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 34:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Chifukwa Yehova ali ndi tsiku lobwezera adani ake,+

      Chaka chopereka chilango chifukwa cha zolakwa zimene Ziyoni anachitiridwa.+

  • Yesaya 35:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Amene ali ndi nkhawa mumtima mwawo muwauze kuti:

      “Limbani mtima. Musachite mantha.

      Chifukwa Mulungu wanu adzabwera nʼkudzabwezera adani anu.

      Mulungu adzabwera kudzapereka chilango.+

      Iye adzabwera ndipo adzakupulumutsani.”+

  • Yesaya 61:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 61 Mzimu wa Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, uli pa ine,+

      Chifukwa Yehova anandidzoza kuti ndilengeze uthenga wabwino kwa anthu ofatsa.+

      Anandituma kuti ndikamange mabala a anthu osweka mtima,

      Kuti ndilengeze za ufulu kwa anthu amene anagwidwa nʼkutengedwa kupita kudziko lina,

      Komanso kuti maso a akaidi adzatsegulidwa.+

       2 Wandituma kuti ndilengeze za chaka cha Yehova chokomera anthu mtima,*

      Ndi za tsiku lobwezera la Mulungu wathu,+

      Komanso kuti nditonthoze anthu onse amene akulira,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena