Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 25:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pa tsiku limenelo anthu akewo adzanena kuti:

      “Taonani! Uyu ndi Mulungu wathu.+

      Chiyembekezo chathu chinali mwa iye+

      Ndipo iye watipulumutsa.+

      Uyu ndi Yehova.

      Chiyembekezo chathu chinali mwa iye.

      Tiyeni tisangalale ndi kukondwera chifukwa watipulumutsa.”+

  • Zefaniya 3:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Tsiku limenelo Yerusalemu adzauzidwa kuti:

      “Usaope iwe Ziyoni,+

      Ndipo manja ako asafooke.

      17 Yehova Mulungu wako ali pakati panu+

      Ndipo adzakupulumutsa chifukwa ndi wamphamvu.

      Iye adzakondwera nawe.+

      Adzakhala phee chifukwa chokhutira ndi chikondi chimene akukusonyeza,

      Ndipo adzafuula mosangalala chifukwa chokondwera nawe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena