Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 51:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Chifukwa Yehova adzatonthoza Ziyoni.+

      Iye adzatonthoza malo ake onse amene anawonongedwa.+

      Adzachititsa chipululu chake kukhala ngati Edeni+

      Ndipo dera lake lachipululu lidzakhala ngati munda wa Yehova.+

      Mwa iye mudzakhala kusangalala ndi kukondwera,

      Kuyamikira ndi kuimba nyimbo zosangalatsa.+

  • Yesaya 56:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Nawonso ndidzawabweretsa kuphiri langa loyera+

      Ndipo ndidzawachititsa kuti asangalale mʼnyumba yanga yopemphereramo.

      Nsembe zawo zopsereza zathunthu ndi nsembe zawo zina ndidzazilandira paguwa langa lansembe.

      Chifukwa nyumba yanga idzatchedwa nyumba yopemphereramo anthu a mitundu yonse.”+

  • Yesaya 65:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Mmbulu ndi mwana wa nkhosa zidzadyera pamodzi,

      Mkango udzadya udzu ngati ngʼombe yamphongo,+

      Ndipo chakudya cha njoka chidzakhala fumbi.

      Zimenezi sizidzapweteka aliyense kapena kuwononga chilichonse mʼphiri langa lonse loyera,”+ akutero Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena