Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 1:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Koresi mfumu ya Perisiya wanena kuti, ‘Yehova Mulungu wakumwamba wandipatsa maufumu onse apadziko lapansi.+ Iye wandituma kuti ndimumangire nyumba ku Yerusalemu+ mʼdziko la Yuda. 3 Aliyense amene ali pakati panu mwa anthu onse amene amamutumikira, Mulungu wake akhale naye ndipo apite ku Yerusalemu mʼdziko la Yuda nʼkukamanganso nyumba ya Yehova Mulungu wa Isiraeli. Iye ndi Mulungu woona ndipo nyumba yake inali ku Yerusalemu.*

  • Yesaya 49:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti:

      “Taona! Ineyo ndidzakwezera dzanja langa mitundu ya anthu,

      Ndipo anthu a mitundu ina ndidzawakwezera chizindikiro.+

      Iwo adzakubweretsera ana ako aamuna atawanyamula mʼmanja,*

      Ndipo ana ako aakazi adzawanyamula paphewa.+

  • Yesaya 62:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Dutsani mʼmageti, dutsani mʼmageti.

      Lambulani njira kuti anthu adutse.+

      Konzani msewu, konzani msewu waukulu.

      Muchotsemo miyala.+

      Anthu a mitundu yosiyanasiyana muwakwezere chizindikiro+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena