Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti anthu a Yehova ndi gawo lake.+

      Yakobo ndiye cholowa chake.+

  • Salimo 115:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova akutikumbukira ndipo adzatidalitsa.

      Adzadalitsa nyumba ya Isiraeli.+

      Adzadalitsa nyumba ya Aroni.

  • Yesaya 61:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Ana awo* adzadziwika pakati pa mitundu ya anthu,+

      Ndipo mbadwa zawo zidzadziwika pakati pa anthu osiyanasiyana.

      Anthu onse owaona adzawazindikira,

      Kuti ndi ana amene* Yehova anawadalitsa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena