Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 32:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Hezekiyatu akukupusitsani pokuuzani kuti: “Yehova Mulungu wathu atipulumutsa mʼmanja mwa mfumu ya Asuri,”+ ndipo mufa ndi njala ndiponso ludzu.

  • 2 Mbiri 32:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Musalole kuti Hezekiya akupusitseni kapena kukusocheretsani chonchi.+ Musamukhulupirire, chifukwa palibe mulungu wa ufumu uliwonse kapena wa mtundu uliwonse amene anatha kupulumutsa anthu ake mʼmanja mwanga ndiponso mʼmanja mwa makolo anga akale. Ndiye mukuganiza kuti Mulungu wanu angakupulumutseni mʼmanja mwanga?’”+

  • Danieli 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndiye ngati ndinu okonzeka kugwada nʼkulambira fano lagolide, mukamva kulira kwa lipenga, chitoliro, zeze wamngʼono, zeze wamakona atatu, choimbira chazingwe, chitoliro chathumba ndi zipangizo zina zonse zoimbira, zili bwino. Koma mukakana kulambira, nthawi yomweyo muponyedwa mungʼanjo yoyaka moto. Ndipo ndi mulungu uti amene angakupulumutseni mʼmanja mwanga?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena