Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 34:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Yehova ali ndi lupanga. Lupangalo lidzakhala magazi okhaokha.

      Lidzakhala mafuta okhaokha,+

      Lidzakhala ndi magazi a nkhosa zamphongo zingʼonozingʼono komanso a mbuzi,

      Lidzakhala ndi mafuta a impso za nkhosa zamphongo.

      Chifukwa Yehova adzapereka nsembe ku Bozira,

      Adzapha nyama zambiri mʼdziko la Edomu.+

  • Yesaya 63:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 63 Kodi amene akuchokera ku Edomuyu+ ndi ndani,

      Amene akuchokera ku Bozira+ atavala zovala zowala zamitundu yosiyanasiyana,*

      Amene zovala zake ndi zaulemelero,

      Ndiponso amene akuyenda ndi mphamvu zake zochuluka?

      “Ndine, amene ndikulankhula mwachilungamo,

      Amene ndili ndi mphamvu zambiri zotha kupulumutsa.”

  • Yeremiya 49:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Taonani! Mofanana ndi chiwombankhanga mdani adzatsika nʼkugwira chakudya chake,+

      Ndipo adzatambasula mapiko ake pa Bozira.+

      Pa tsiku limenelo mtima wa asilikali a ku Edomu

      Udzakhala ngati mtima wa mkazi amene akubereka.”

  • Amosi 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Choncho ndidzatumiza moto ku Temani,+

      Ndipo udzawotcheratu nsanja zolimba za ku Bozira.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena