Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 29:31, 32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 “Anthu onse amene ali ku ukapolo uwatumizire uthenga wakuti, ‘Ponena za Semaya wa ku Nehelamu, Yehova wanena kuti: “Popeza Semaya analosera kwa inu, ngakhale kuti ine sindinamutume ndipo anayesetsa kukuchititsani kuti mukhulupirire zinthu zabodza,+ 32 Yehova wanena kuti, ‘Ine ndilanga Semaya wa ku Nehelamu ndi mbadwa zake. Sipadzapezeka mwamuna aliyense wochokera mʼbanja lake amene adzapulumuke pakati pa anthu awa. Ndipo iye sadzaona zabwino zimene ndidzachitire anthu anga chifukwa walimbikitsa anthu kuti apandukire Yehova,’ akutero Yehova.”’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena