Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 10:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kerubi aliyense anali ndi nkhope 4. Nkhope yoyamba inali ya kerubi. Nkhope yachiwiri inali ya munthu. Nkhope yachitatu inali ya mkango ndipo nkhope ya 4 inali ya chiwombankhanga.+

      15 Akerubiwo anali angelo omwe aja amene ndinawaona kumtsinje wa Kebara.+ Akerubiwo akanyamuka kukwera mʼmwamba

  • Chivumbulutso 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mngelo woyamba ankaoneka ngati mkango.+ Mngelo wachiwiri ankaoneka ngati mwana wa ngʼombe wamphongo.+ Mngelo wachitatu+ anali ndi nkhope yooneka ngati ya munthu ndipo mngelo wa 4+ ankaoneka ngati chiwombankhanga chimene chikuuluka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena