Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 10:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ana a Semu anali Elamu,+ Ashuri,+ Aripakisadi,+ Ludi ndi Aramu.+

  • Yesaya 11:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pa tsiku limenelo Yehova adzaperekanso dzanja lake kachiwiri kuti atenge anthu ake otsala kuchokera ku Asuri,+ ku Iguputo,+ ku Patirosi,+ ku Kusi,+ ku Elamu,+ ku Sinara,* ku Hamati ndi mʼzilumba zamʼnyanja.+

  • Yesaya 21:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndauzidwa masomphenya ochititsa mantha akuti:

      Mtundu wachinyengo ukuchita zachinyengo,

      Ndipo mtundu wowononga ukuwononga.

      Pita ukachite nkhondo, iwe Elamu! Kazungulire mzindawo, iwe Mediya!+

      Ndidzathetsa mavuto onse amene mzindawo unachititsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena