Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 4:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Amenewa ndi maloto amene ine Mfumu Nebukadinezara ndinalota. Tsopano iwe Belitesazara umasulire malotowa, chifukwa amuna ena onse anzeru a mu ufumu wanga alephera kundiuza kumasulira kwake.+ Koma iwe ungathe kuwamasulira chifukwa mzimu wa milungu yoyera uli mwa iwe.’

  • Danieli 5:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mu ufumu wanu muli munthu amene ali ndi mzimu wa milungu yoyera. Mʼmasiku a bambo anu, anthu anazindikira kuti munthuyu ndi wodziwa zinthu kwambiri, wozindikira ndiponso ali ndi nzeru zofanana ndi nzeru za milungu.+ Ndiyeno bambo anu, Mfumu Nebukadinezara, anamuika kuti akhale mkulu wa ansembe ochita zamatsenga, anthu okhulupirira mizimu, Akasidi* ndi anthu okhulupirira nyenyezi.+ Ndithudi mfumu, bambo anu anamupatsa udindo umenewu. 12 Anachita zimenezi chifukwa Danieli, amene mfumu inamupatsa dzina lakuti Belitesazara,+ anali ndi luso lodabwitsa, anali wodziwa zinthu ndi wozindikira pa nkhani yomasulira maloto, kumasulira mikuluwiko komanso kuthana ndi zinthu zovuta.*+ Tsopano itanani Danieli ndipo akuuzani kumasulira kwa mawu amenewa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena