-
Levitiko 7:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 Munthu akakhudza chilichonse chodetsedwa, kaya ndi chodetsa chochokera kwa munthu+ kapena nyama yodetsedwa,+ kapenanso chinthu chilichonse chonyansa chodetsedwa,+ nʼkudya ina mwa nyama ya nsembe yamgwirizano, imene ndi ya Yehova, munthu ameneyo aziphedwa kuti asakhalenso pakati pa anthu a mtundu wake.’”
-