Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Iye adzawauza kuti: “Inetu ndasankha mfumu yanga+

      Ndipo ikulamulira ku Ziyoni,+ phiri langa lopatulika.”

  • Yesaya 32:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Taonani! Mfumu+ idzalamulira mwachilungamo,+

      Ndipo akalonga adzalamuliranso mwachilungamo.

  • Yeremiya 23:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Taonani! Masiku adzafika,” watero Yehova, “pamene ndidzaike mfumu yolungama pampando wachifumu yochokera mʼbanja lachifumu la Davide.*+ Mfumuyo idzalamulira mʼdzikoli+ ndipo idzachita zinthu mwanzeru, motsatira malamulo komanso mwachilungamo.+

  • Luka 19:37, 38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Atangofika pafupi ndi msewu wochokera mʼphiri la Maolivi, gulu lonse la ophunzirawo linayamba kusangalala ndi kutamanda Mulungu mokweza mawu chifukwa cha ntchito zonse zamphamvu zimene anaona. 38 Iwo ankanena kuti: “Wodalitsidwa ndi amene akubwera monga Mfumu mʼdzina la Yehova!* Mtendere kumwamba ndi ulemerero kumwambamwambako!”+

  • Yohane 1:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Natanayeli anamuyankha kuti: “Rabi, ndinu Mwana wa Mulungu, ndinu Mfumu ya Isiraeli.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena