Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 66:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chifukwa inu Mulungu mwatifufuza.+

      Mwatiyenga ngati mmene amayengera siliva.

  • Miyambo 25:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yengani siliva nʼkuchotsa zonse zosafunika,

      Ndipo yense adzatuluka woyengeka bwino.+

  • Zekariya 13:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 “Ine ndidzatenga anthu otsalawo nʼkuwaika pamoto.

      Ndipo ndidzawayenga ngati mmene amayengera siliva

      Komanso kuwayesa ngati mmene amayesera golide.+

      Iwo adzaitana dzina langa,

      Ndipo ine ndidzawayankha.

      Ndidzanena kuti, ‘Awa ndi anthu anga,’+

      Ndipo iwo adzanena kuti, ‘Yehova ndi Mulungu wathu.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena