Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 6:47-49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Aliyense amene amabwera kwa ine kudzamva mawu anga, nʼkuchita zimene wamvazo, ndikuuzani amene amafanana naye:+ 48 Iyeyo ali ngati munthu amene pomanga nyumba, anakumba mozama kwambiri nʼkuyala maziko pathanthwe. Ndiye mtsinje utasefukira, madzi anawomba nyumbayo, koma sanathe kuigwedeza chifukwa anaimanga bwino.+ 49 Pamene munthu amene wamva koma osachita chilichonse,+ ali ngati munthu amene wamanga nyumba yopanda maziko padothi. Apanso mtsinje unasefukira nʼkuwomba nyumbayo, ndipo nthawi yomweyo inagwa, moti kugwa kwake kunali kwakukulu.”

  • Yakobo 1:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma amene amayangʼanitsitsa mulamulo langwiro+ limene limabweretsa ufulu ndipo amapitiriza kuliyangʼanitsitsa, adzakhala wosangalala ndi zimene akuchita+ chifukwa chakuti si munthu amene amangomva nʼkuiwala, koma amene amachita zimene wamvazo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena