Yesaya 53:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Tonsefe tikungoyendayenda uku ndi uku ngati nkhosa zosochera.+Aliyense akulowera njira yakeNdipo Yehova wachititsa kuti zolakwa za tonsefe zigwere pa ameneyo.+ Mateyu 10:5, 6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Yesu anatumiza atumwi 12 amenewa ndipo anawapatsa malangizo awa:+ “Musapite mumsewu wa anthu a mitundu ina ndipo musalowe mumzinda uliwonse wa Asamariya.+ 6 Mʼmalomwake, nthawi zonse muzipita kwa nkhosa zosochera za nyumba ya Isiraeli.+ Machitidwe 3:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Mulungu atasankha Mtumiki wake, choyamba+ anamutumiza kwa inu, kuti adzakudalitseni pobweza aliyense wa inu kuti musiye ntchito zanu zoipa.” Machitidwe 13:46 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 46 Choncho Paulo ndi Baranaba analankhula molimba mtima kuti: “Inu munali oyenera kuti muyambe kuuzidwa mawu a Mulungu.+ Koma popeza mukuwakana ndipo mukudziweruza nokha kuti ndinu osayenera moyo wosatha, ife tikupita kwa anthu a mitundu ina.+ Aroma 15:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Kunena zoona, Khristu anakhala mtumiki wa anthu odulidwa+ kuti atsimikizire kuti Mulungu ndi wokhulupirika posonyeza kuti malonjezo amene Mulunguyo anapatsa makolo awo ndi otsimikizirika.+
6 Tonsefe tikungoyendayenda uku ndi uku ngati nkhosa zosochera.+Aliyense akulowera njira yakeNdipo Yehova wachititsa kuti zolakwa za tonsefe zigwere pa ameneyo.+
5 Yesu anatumiza atumwi 12 amenewa ndipo anawapatsa malangizo awa:+ “Musapite mumsewu wa anthu a mitundu ina ndipo musalowe mumzinda uliwonse wa Asamariya.+ 6 Mʼmalomwake, nthawi zonse muzipita kwa nkhosa zosochera za nyumba ya Isiraeli.+
26 Mulungu atasankha Mtumiki wake, choyamba+ anamutumiza kwa inu, kuti adzakudalitseni pobweza aliyense wa inu kuti musiye ntchito zanu zoipa.”
46 Choncho Paulo ndi Baranaba analankhula molimba mtima kuti: “Inu munali oyenera kuti muyambe kuuzidwa mawu a Mulungu.+ Koma popeza mukuwakana ndipo mukudziweruza nokha kuti ndinu osayenera moyo wosatha, ife tikupita kwa anthu a mitundu ina.+
8 Kunena zoona, Khristu anakhala mtumiki wa anthu odulidwa+ kuti atsimikizire kuti Mulungu ndi wokhulupirika posonyeza kuti malonjezo amene Mulunguyo anapatsa makolo awo ndi otsimikizirika.+