Luka 21:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Tsoka kwa akazi oyembekezera komanso oyamwitsa ana mʼmasiku amenewo!+ Chifukwa mʼdzikoli mudzakhala mavuto aakulu komanso mkwiyo pa anthu awa. Chivumbulutso 7:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Nthawi yomweyo, ndinamuyankha kuti: “Mbuyanga, mukudziwa ndinu.” Ndipo iye anandiuza kuti: “Amenewa ndi amene atuluka mʼchisautso chachikulu+ ndipo achapa mikanjo yawo nʼkuiyeretsa mʼmagazi a Mwanawankhosa.+
23 Tsoka kwa akazi oyembekezera komanso oyamwitsa ana mʼmasiku amenewo!+ Chifukwa mʼdzikoli mudzakhala mavuto aakulu komanso mkwiyo pa anthu awa.
14 Nthawi yomweyo, ndinamuyankha kuti: “Mbuyanga, mukudziwa ndinu.” Ndipo iye anandiuza kuti: “Amenewa ndi amene atuluka mʼchisautso chachikulu+ ndipo achapa mikanjo yawo nʼkuiyeretsa mʼmagazi a Mwanawankhosa.+