Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 1:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Nthawi yomweyo mzimuwo unamulimbikitsa kuti apite kuchipululu. 13 Choncho iye anakhala mʼchipululumo masiku 40, akuyesedwa ndi Satana.+ Mʼchipululumo munalinso nyama zakutchire ndipo angelo ankamutumikira.+

  • Luka 4:1-4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako Yesu anachoka ku Yorodano atadzazidwa ndi mzimu woyera ndipo mzimuwo unamutenga nʼkumuyendetsa malo osiyanasiyana mʼchipululu+ 2 kwa masiku 40, kumene ankayesedwa ndi Mdyerekezi.+ Pa masiku amenewo sanadye chilichonse ndipo masikuwo atatha, anamva njala. 3 Mdyerekezi ataona zimenezi anamuuza kuti: “Ngati ndinu mwana wa Mulungu, uzani mwala uwu kuti usanduke mkate.” 4 Koma Yesu anamuyankha kuti: “Malemba amati, ‘Munthu sangakhale ndi moyo ndi chakudya chokha.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena