Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 15:35, 36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ena mwa anthu amene anaimirira chapafupi atamva zimenezo anayamba kunena kuti: “Tamverani! Akuitana Eliya.” 36 Kenako wina anathamanga kukaviika siponji muvinyo wowawasa ndipo anaiika kubango nʼkumupatsa kuti amwe.+ Iye ananena kuti: “Mulekeni! Tione ngati Eliya angabwere kudzamutsitsa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena