Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 4:42-44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Ndiyeno kunabwera munthu wina kuchokera ku Baala-salisa.+ Iye anabweretsera munthu wa Mulungu woonayo mikate 20 ya balere+ woyambirira kucha komanso thumba la tirigu* watsopano.+ Kenako Elisa anati: “Apatse anthuwa kuti adye.” 43 Koma mtumiki wakeyo anati: “Ndingagawire bwanji anthu 100 chakudya chimenechi?”+ Elisa anati: “Agawire anthuwa kuti adye chifukwa Yehova wanena kuti, ‘Anthu adya nʼkukhuta ndipo china chitsala.’”+ 44 Atamva zimenezi, anagawira anthuwo chakudyacho. Iwo anadya ndipo china chinatsala+ mogwirizana ndi mawu a Yehova.

  • Mateyu 15:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Koma ophunzirawo anamuuza kuti: “Kumalo kopanda anthu ngati kuno chakudya chokwanira gulu lonseli tichipeza kuti?”+

  • Yohane 6:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Filipo anamuyankha kuti: “Mitanda ya mkate ya ndalama zokwana madinari 200* singawakwanire ngakhale titati aliyense angolandirako pangʼono.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena