Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 12:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yesu atadziwa zimenezi, anachoka pamalo amenewo. Anthu ambiri anamutsatira+ ndipo iye anawachiritsa onsewo, 16 koma anawalamula mwamphamvu kuti asamuulule.+

  • Maliko 8:29, 30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Ndiyeno anafunsa ophunzirawo kuti: “Nanga inuyo mumati ndine ndani?” Petulo anayankha kuti: “Ndinu Khristu.”+ 30 Atanena zimenezo, anawalamula mwamphamvu kuti asauze aliyense za iye.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena