Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 5:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Inu ndinu mchere+ wa dziko lapansi. Koma ngati mchere watha mphamvu, kodi mphamvu yakeyo angaibwezeretse bwanji? Sungagwirenso ntchito iliyonse koma ungafunike kungoutaya kunja+ kuti anthu azikaupondaponda.

  • Luka 14:34, 35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Kunena zoona, mchere ndi wabwino. Koma ngati mcherewo watha mphamvu, kodi mphamvu yakeyo ingabwezeretsedwe bwanji?+ 35 Ndi wosayenera kuuthira munthaka kapena mʼmanyowa. Anthu amangoutaya kunja. Amene ali ndi makutu akumva, amve.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena