Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 14:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Atauza anthuwo kuti azipita, anakwera phiri yekhayekha kukapemphera.+ Iye anakhala kumeneko yekhayekha mpaka kunja kunada.

  • Maliko 14:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Kenako anafika pamalo otchedwa Getsemane ndipo anauza ophunzira akewo kuti: “Khalani pansi panopa, ine ndikukapemphera.”+

  • Luka 4:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Kutacha, anachoka nʼkupita kumalo kopanda anthu.+ Koma gulu la anthu linayamba kumufunafuna mpaka linafika kumene iye anali, ndipo anthuwo anamupempha kuti asachoke.

  • Aheberi 5:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pamene Khristu anali padzikoli,* anapereka mapemphero ochonderera ndiponso opempha, kwa amene akanatha kumupulumutsa ku imfa. Anapereka mapempherowa mofuula komanso akugwetsa misozi,+ ndipo anamumvera chifukwa ankaopa Mulungu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena