Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 26:36, 37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kenako Yesu anafika nawo pamalo otchedwa Getsemane,+ ndipo anauza ophunzirawo kuti: “Khalani pansi panopa, ine ndikupita uko kukapemphera.”+ 37 Popita kumeneko anatenga Petulo ndi ana awiri a Zebedayo. Ndipo anayamba kumva chisoni komanso kuvutika kwambiri mumtima mwake.+

  • Luka 22:39-41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Atachoka kumeneko anapita kuphiri la Maolivi ngati mmene ankachitira nthawi zonse ndipo ophunzira ake nawonso anamutsatira.+ 40 Atafika pamalowo anauza ophunzirawo kuti: “Pitirizani kupemphera kuti musalowe mʼmayesero.”+ 41 Iye anachoka pamene panali ophunzirawo nʼkuyenda kamtunda, kutalika kwake ngati pamene pangagwere mwala munthu atauponya. Kumeneko anagwada nʼkuyamba kupemphera

  • Yohane 18:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Atamaliza kunena zinthu zimenezi, Yesu anatuluka limodzi ndi ophunzira ake nʼkuwoloka chigwa cha Kidironi+ kupita kumene kunali munda. Iye ndi ophunzira akewo analowa mʼmundamo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena