-
Yakobo 1:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 Munthu akakhala pa mayesero asamanene kuti: “Mulungu akundiyesa.” Chifukwa Mulungu sangayesedwe ndi zinthu zoipa ndipo iye sayesa munthu ndi zinthu zoipa.
-