Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 12:31, 32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Pa chifukwa chimenechi ndikukuuzani kuti, anthu adzakhululukidwa tchimo la mtundu uliwonse ndi mawu aliwonse onyoza, koma wonyoza mzimu sadzakhululukidwa.+ 32 Mwachitsanzo, aliyense wolankhula mawu onyoza Mwana wa munthu, adzakhululukidwa.+ Koma aliyense wolankhula mawu onyoza mzimu woyera, sadzakhululukidwa, mʼnthawi* ino kapena ikubwerayo.+

  • Maliko 3:28, 29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ndithu ndikukuuzani, ana a anthu adzakhululukidwa zinthu zonse, kaya anachita machimo otani kapena analankhula mawu onyoza bwanji. 29 Koma aliyense amene wanyoza mzimu woyera sadzakhululukidwa kwamuyaya,+ koma adzakhala ndi mlandu wa tchimo losatha.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena