Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 1:20, 21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma ataganizira mozama za nkhani imeneyi, mngelo wa Yehova* anamuonekera mʼmaloto nʼkumuuza kuti: “Yosefe, mwana wa Davide, usaope kutenga Mariya mkazi wako nʼkupita naye kunyumba, popeza iye ndi woyembekezera chifukwa cha mphamvu ya mzimu woyera.+ 21 Iye adzabereka mwana wamwamuna ndipo udzamupatse dzina lakuti Yesu,*+ chifukwa adzapulumutsa anthu ake ku machimo awo.”+

  • Luka 1:30, 31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Choncho mngeloyo anamuuza kuti: “Usaope Mariya, chifukwa Mulungu wakukomera mtima. 31 Tsopano mvetsera! Udzakhala woyembekezera nʼkubereka mwana wamwamuna+ ndipo udzamupatse dzina lakuti Yesu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena