Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 12:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsiku limeneli lidzakhala chikumbutso kwa inu, ndipo muzichitira Yehova chikondwerero mʼmibadwo yanu yonse. Limeneli ndi lamulo mpaka kalekale, kuti muzichita chikondwerero chimenechi.

  • Ekisodo 12:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mʼmwezi woyamba, tsiku la 14 la mwezi umenewo, madzulo muzidzadya mikate yopanda zofufumitsa, mpaka kukafika madzulo a tsiku la 21 mwezi womwewo.+

  • Deuteronomo 16:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Muzikumbukira kuti mwezi wa Abibu* ndi wofunika ndipo muzichita chikondwerero cha Pasika kwa Yehova Mulungu wanu,+ chifukwa mʼmwezi wa Abibu Yehova Mulungu wanu anakutulutsani mu Iguputo usiku.+ 2 Ndipo muzipereka nsembe ya Pasika kwa Yehova Mulungu wanu.+ Muzipereka nkhosa ndi ngʼombe+ pamalo amene Yehova adzasankhe kuikapo dzina lake.+

  • Mateyu 26:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pa tsiku loyamba la chikondwerero cha Mikate Yopanda Zofufumitsa,+ ophunzira anabwera kwa Yesu nʼkumufunsa kuti: “Kodi mukufuna tikakukonzereni kuti malo odyerako Pasika?”+

  • Maliko 14:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa tsiku loyamba la chikondwerero cha Mikate Yopanda Zofufumitsa,+ pamene mwamwambo ankapereka nsembe nyama ya Pasika,+ ophunzira ake anamufunsa kuti: “Kodi mukufuna tikakukonzereni kuti malo odyerako Pasika?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena