Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 18:25-27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Pa nthawiyi Simoni Petulo anali ataima pomwepo nʼkumawotha moto. Ndiyeno iwo anamufunsa kuti: “Kodi iwenso si mmodzi wa ophunzira ake?” Iye anakana nʼkunena kuti: “Ayi si ine.”+ 26 Mmodzi wa akapolo a mkulu wa ansembe, amenenso anali wachibale wa munthu amene Petulo anamudula khutu uja,+ anati: “Ndinakuona mʼmunda muja uli naye limodzi, ndikunama kapena?” 27 Koma Petulo anakananso ndipo nthawi yomweyo tambala analira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena