Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 28:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tsiku la Sabata litatha, mʼbandakucha wa tsiku loyamba la mlunguwo, Mariya wa ku Magadala ndi Mariya wina uja anabwera kudzaona manda.+

  • Mateyu 28:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Choncho iwo anachoka mwamsanga pamandapo ali ndi mantha ndiponso chimwemwe chochuluka ndipo anathamanga kukauza ophunzira ake.+

  • Luka 24:9-11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 ndipo anachoka kumandako* nʼkubwerera kukanena zonsezi kwa ophunzira 11 aja ndi kwa ena onse.+ 10 Azimayiwa anali Mariya wa ku Magadala, Jowana ndi Mariya amayi ake a Yakobo. Komanso azimayi ena onse amene anali nawo limodzi ankauza atumwi zinthu zimenezi. 11 Koma kwa iwo, zimene ankawauzazo zinkaoneka ngati zopanda pake ndipo sanawakhulupirire azimayiwo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena