Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Onse amene akutsogoleredwa ndi mzimu wa Mulungu, ndi anadi a Mulungu.+

  • Aroma 8:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mzimuwo umachitira umboni limodzi ndi mzimu wathu+ kuti ndife ana a Mulungu.+

  • 2 Akorinto 6:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “‘Ndidzakhala bambo anu+ ndipo inu mudzakhala ana anga aamuna ndi aakazi,’+ watero Yehova* Wamphamvuyonse.”

  • Aefeso 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Chifukwa anatisankhiratu+ kuti adzatitenga nʼkukhala ana ake+ kudzera mwa Yesu Khristu, mogwirizana ndi zimene zinamusangalatsa komanso zimene anafuna.+

  • 1 Yohane 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Taganizirani za chikondi chachikulu chimene Atate watisonyeza+ potitchula kuti ana ake.*+ Ndipo ndifedi ana ake. Nʼchifukwa chake dziko silikutidziwa,+ popeza iyeyo silikumudziwanso.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena