Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 8:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ine ndinali woyamba kulengedwa ndi Yehova,+

      Ndinali woyambirira pa zinthu zonse zimene anapanga kalekale kwambiri.+

  • Yohane 17:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiye tsopano Atate, ndiloleni kuti ndikhale pambali panu ndipo mundipatse ulemerero umene ndinali nawo pambali panu dziko lisanakhalepo.+

  • Afilipi 2:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ngakhale kuti iye ankaoneka ngati Mulungu,+ sanaganizirepo zoti ayese kulanda udindo wa Mulungu kuti akhale wofanana naye.+ 7 Ayi sanachite zimenezo, koma anasiya zonse zimene anali nazo nʼkukhala ngati kapolo+ ndipo anakhala munthu.*+

  • Akolose 1:15-17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iye ndi chifaniziro cha Mulungu wosaonekayo,+ woyamba kubadwa wa chilengedwe chonse.+ 16 Kudzera mwa iye, Mulungu analenga zinthu zina zonse kumwamba ndi padziko lapansi. Analenga zinthu zooneka ndi zinthu zosaoneka,+ kaya ndi mipando yachifumu, ambuye, maboma komanso maulamuliro. Inde, analenga zinthu zina zonse kudzera mwa iye+ ndiponso chifukwa cha iye. 17 Ndiponso iye analipo kale zinthu zina zonse zisanakhaleko+ ndipo zinthu zina zonse zinakhalapo kudzera mwa iye.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena