Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 26:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Zimene mayiyu wachita pothira mafuta onunkhirawa pathupi langa, wazichita pokonzekera kuikidwa mʼmanda kwanga.+

  • Maliko 14:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mayiyu wachita zimene akanatha. Iye wathiriratu mafuta onunkhira pathupi langa pokonzekera kuikidwa mʼmanda kwanga.+

  • Yohane 19:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Choncho iwo anatenga mtembo wa Yesu nʼkuukulunga ndi nsalu zamaliro zonunkhira,+ mogwirizana ndi mwambo umene Ayuda ankatsatira poika maliro.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena