Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 89:35, 36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ndalumbira kamodzi kokha pa kuyera kwanga.

      Davide sindidzamunamiza.+

      36 Mbadwa* zake zidzakhalapo mpaka kalekale,+

      Ndipo mpando wake wachifumu udzakhala pamaso panga kwamuyaya ngati dzuwa.+

  • Salimo 110:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yehova walumbira ndipo sadzasintha maganizo. Iye wati:

      “Iwe ndiwe wansembe mpaka kalekale,+

      Mofanana ndi unsembe wa Melekizedeki!”+

  • Yesaya 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ulamuliro* wake udzafika kutali

      Ndipo mtendere sudzatha,+

      Pampando wachifumu wa Davide+ ndiponso mu ufumu wake

      Kuti iye achititse ufumuwo kukhazikika+ ndiponso kukhala wolimba

      Pogwiritsa ntchito chilungamo+ ndiponso mtima wowongoka,+

      Kuyambira panopa mpaka kalekale.

      Yehova wa magulu ankhondo akumwamba adzachita zimenezi modzipereka kwambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena