Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 28:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Yakobo anachoka ku Beere-seba nʼkupitiriza ulendo wake wopita ku Harana.+

  • Genesis 28:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kenako anayamba kulota. Mʼmalotowo anaona masitepe* ochokera padziko lapansi mpaka kumwamba, angelo a Mulungu akukwera ndi kutsika pamasitepewo.+

  • Salimo 104:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iye amachititsa kuti angelo ake akhale amphamvu,*

      Amachititsa atumiki ake kuti akhale moto wopsereza.+

  • Danieli 7:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndinapitiriza kuona masomphenya usikuwo ndipo ndinaona winawake wooneka ngati mwana wa munthu+ akubwera mʼmitambo. Iye analoledwa kufika kwa Wamasiku Ambiri+ uja ndipo anamubweretsa pafupi kwambiri ndi Wamasiku Ambiriyo.

  • Mateyu 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kenako Mdyerekezi uja anamusiya+ ndipo kunabwera angelo nʼkuyamba kumutumikira.+

  • Luka 22:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Atatero mngelo wochokera kumwamba anaonekera kwa iye nʼkumulimbikitsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena