Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 6:68
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 68 Simoni Petulo anayankha kuti: “Ambuye, tingapitenso kwa ndani?+ Inu ndi amene muli ndi mawu othandiza munthu kuti adzapeze moyo wosatha.+

  • Yohane 8:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Kenako Yesu anati: “Mukadzamukweza Mwana wa munthu,+ pamenepo mudzadziwa kuti amene munkamuyembekezera uja ndi ine+ komanso kuti sindichita chilichonse mongoganiza ndekha.+ Koma zimene ndimalankhula zimakhala zogwirizana ndendende ndi zimene Atate anandiphunzitsa.

  • Yohane 12:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Chifukwa sindinalankhulepo zongoganiza pandekha, koma Atate amene ananditumawo anandipatsa lamulo pa zimene ndiyenera kunena ndi zimene ndiyenera kulankhula.+

  • Yohane 14:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kodi sukukhulupirira kuti Atate ndi ine ndife ogwirizana?+ Zinthu zimene ndimakuuzani sindilankhula zamʼmaganizo mwanga,+ koma Atate amene ndi wogwirizana ndi ine ndi amene akuchita ntchito zake kudzera mwa ine.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena