Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 26:55
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 Mu ola lomwelo Yesu anafunsa gulu la anthulo kuti: “Bwanji mwabwera kudzandigwira mutatenga malupanga ndi zibonga ngati mukudzalimbana ndi wachifwamba? Tsiku ndi tsiku ndinkakhala pansi mʼkachisi nʼkumaphunzitsa,+ koma simunandigwire.+

  • Luka 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Komanso anayamba kuphunzitsa mʼmasunagoge awo ndipo anthu onse ankamulemekeza.

  • Luka 19:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Ndipo tsiku ndi tsiku iye anapitiriza kuphunzitsa mʼkachisimo. Koma ansembe aakulu, alembi ndi akuluakulu a anthu ankafunitsitsa kumupha.+

  • Yohane 7:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Chikondwererocho chitafika pakatikati, Yesu analowa mʼkachisi ndipo anayamba kuphunzitsa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena