Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 27:59, 60
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 59 Yosefe anatenga mtembowo nʼkuukulunga munsalu yoyera yabwino kwambiri,+ 60 ndipo anakauika mʼmanda*+ ake atsopano amene anawasema muthanthwe. Kenako atagubuduza chimwala chachikulu nʼkutseka pakhomo la mandawo,* anachoka.

  • Yohane 19:40-42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Choncho iwo anatenga mtembo wa Yesu nʼkuukulunga ndi nsalu zamaliro zonunkhira,+ mogwirizana ndi mwambo umene Ayuda ankatsatira poika maliro. 41 Tsopano kumalo kumene anamupachikirako kunali munda mmene munali manda* atsopano,+ ndipo anali asanaikemo munthu chiyambire. 42 Popeza linali Tsiku Lokonzekera+ Chikondwerero cha Ayuda, ndipo mandawo anali pafupi, iwo anaika Yesu mmenemo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena