Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 10:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Ndiponso aliyense amene sakufuna kunyamula mtengo wake wozunzikirapo* nʼkupitiriza kunditsatira ndi wosayenera kuti akhale wophunzira wanga.+

  • Yohane 15:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mukanakhala mbali ya dziko, dziko likanakukondani monga mbali yake. Popeza simuli mbali ya dzikoli,+ koma ine ndinakusankhani kuchokera mʼdziko, pa chifukwa chimenechi dziko likudana nanu.+

  • Aroma 8:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho ngati tili ana, ndifenso olandira cholowa kuchokera kwa Mulungu. Koma ndifenso olandira cholowa+ anzake a Khristu, ngati tikuvutika naye limodzi+ kuti tikalandire naye ulemerero.+

  • 1 Atesalonika 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Chifukwa pamene tinali nanu limodzi, tinkakuuziranitu kuti tidzakumana ndi mavuto ndipo monga mmene mukudziwira, zimene tinkakuuzanizo ndi zimene zachitikadi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena