Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 10:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Mayina a atumwi 12 ndi awa:+ Simoni, amene ankatchulidwa kuti Petulo*+ ndi Andireya+ mchimwene wake. Yakobo mwana wa Zebedayo ndi mchimwene wake Yohane.+

  • Machitidwe 11:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Iye anatiuza kuti ali mʼnyumba mwake anaona mngelo ataimirira ndipo anamuuza kuti, ‘Tuma anthu kuti apite ku Yopa akaitane Simoni wotchedwanso Petulo.+

  • 2 Petulo 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Ndine Simoni Petulo, kapolo komanso mtumwi wa Yesu Khristu. Ndikulembera anthu amene apeza chikhulupiriro chamtengo wapatali chofanana ndi chathu kudzera mʼchilungamo cha Mulungu wathu ndiponso cha Mpulumutsi wathu Yesu Khristu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena