Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 19:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndiyeno Pilato anamuuza kuti: “Kodi sukufuna kulankhula nane? Kodi sukudziwa kuti ndili ndi mphamvu zokumasula komanso zokupachika?”* 11 Yesu anamuyankha kuti: “Simukanakhala ndi mphamvu iliyonse pa ine mukanapanda kupatsidwa kuchokera kumwamba. Nʼchifukwa chake munthu amene wandipereka kwa inu ali ndi tchimo lalikulu kwambiri.”

  • Machitidwe 4:27, 28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Zimenezi zinachitikadi pamene Herode, Pontiyo Pilato,+ anthu a mitundu ina komanso anthu a mu Isiraeli, anasonkhana mumzindawu nʼkuukira Yesu, mtumiki wanu woyera, amene inu munamudzoza.+ 28 Anasonkhana kuti achite zimene munaneneratu. Zimenezi zinachitika chifukwa inu muli ndi mphamvu komanso chifukwa zinali zogwirizana ndi chifuniro chanu.+

  • 1 Petulo 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Zoonadi, Mulungu anasankhiratu Khristu anthu asanayambe kuberekana padziko lapansi,+ koma anaonekera pa nthawi yamapeto chifukwa cha inuyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena