Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 6:56
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 56 Ndipo akangolowa mʼmidzi kapena mʼmizinda komanso mʼmadera ozungulira, anthu ankakhazika odwala mʼmisika. Iwo ankamuchonderera kuti angogwira ulusi wopota wamʼmphepete mwa malaya ake akunja,+ ndipo anthu onse amene anaugwira anachira.

  • Machitidwe 5:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Anthuwo ankabweretsa odwala mʼmisewu nʼkuwagoneka pamabedi angʼonoangʼono ndi pamphasa kuti Petulo akamadutsa, chithunzithunzi chake chokha chifike pa ena mwa odwalawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena