Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 14:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ine ndidzapempha Atate ndipo adzakupatsani mthandizi* wina kuti adzakhale nanu mpaka kalekale.+ 17 Mthandizi ameneyo ndi mzimu wa choonadi+ umene dziko silingaulandire, chifukwa siliuona kapena kuudziwa.+ Inu mumaudziwa chifukwa umakhala mwa inu ndipo uli mwa inu.

  • Machitidwe 2:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Iye anakwezedwa nʼkukhala kudzanja lamanja la Mulungu+ ndipo analandira mzimu woyera wolonjezedwawo kuchokera kwa Atate.+ Choncho iye watipatsa* mzimu woyera umene mukuuona ndi kuumvawu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena