Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 51:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Taonani! Ndinabadwa ndili wochimwa,

      Ndipo ndine wochimwa kuchokera pamene mayi anga anatenga pakati panga.+

  • Yohane 8:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Yesu anawayankha kuti: “Ndithudi ndikukuuzani, aliyense amene akuchita tchimo ndi kapolo wa tchimo.+

  • Aroma 6:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kodi simukudziwa kuti mukamadzipereka kwa winawake ngati akapolo omvera, mumakhala akapolo a amene mukumumverayo?+ Mumakhala akapolo a uchimo+ umene umatsogolera ku imfa,+ kapena akapolo a kumvera komwe kumatsogolera ku chilungamo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena