Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 53:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Anapatsidwa manda* limodzi ndi anthu oipa,+

      Ndipo pamene anafa anaikidwa mʼmanda limodzi ndi anthu olemera,*+

      Ngakhale kuti iye sanalakwe chilichonse*

      Ndipo mʼkamwa mwake munalibe chinyengo.+

  • Mateyu 27:59, 60
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 59 Yosefe anatenga mtembowo nʼkuukulunga munsalu yoyera yabwino kwambiri,+ 60 ndipo anakauika mʼmanda*+ ake atsopano amene anawasema muthanthwe. Kenako atagubuduza chimwala chachikulu nʼkutseka pakhomo la mandawo,* anachoka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena