Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 9:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Munthu aliyense wochita nawo mpikisano amakhala wodziletsa pa zinthu zonse. Anthu amachita zimenezo kuti akalandire nkhata yakumutu imene imawonongeka,+ koma ife, kuti tikapeze nkhata yakumutu yomwe singawonongeke.+

  • Yakobo 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Wosangalala ndi munthu amene akupirira mayesero,+ chifukwa akadzavomerezedwa, adzalandira mphoto* ya moyo,+ imene Yehova* analonjeza onse amene akupitiriza kumukonda.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena