Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Iye anawauza kuti: “Mukamathandiza amayi a Chiheberi kubereka+ ndipo mwaona kuti mwana amene akubadwayo ndi wamwamuna muzimupha, koma ngati ndi wamkazi muzimusiya wamoyo.”

  • Ekisodo 1:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kenako Farao analamula anthu ake onse kuti: “Mwana aliyense wamwamuna wobadwa kumene wa Aheberi muzimuponya mumtsinje wa Nailo, koma mwana aliyense wamkazi muzimusiya wamoyo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena