Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 9:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kodi simukudziwa kuti ochita mpikisano wothamanga amathamanga onse, koma amene amakalandira mphoto ndi mmodzi yekha? Muzithamanga mʼnjira yoti mukalandire mphotoyo.+

  • 1 Akorinto 9:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Choncho sikuti ndikungothamanga osadziwa kumene ndikupita.+ Mmene ndikuponyera zibakera zanga, sikuti ndikungomenya mphepo ayi.

  • Afilipi 3:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Abale, ine sindikudziona ngati ndalandira kale mphotoyo ayi. Koma pali chinthu chimodzi chimene ndikuchita: Ndikuiwala zinthu zakumbuyo+ ndipo ndikuyesetsa kuti ndikapeze zakutsogolo.+ 14 Ndikuyesetsa kuti ndikwaniritse cholinga changa chokalandira mphoto.+ Mphoto imeneyi ndi kukakhala ndi moyo kumwamba+ ndipo Mulungu adzaipereka kwa anthu amene anawaitana kudzera mwa Khristu Yesu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena